
ndileke - lulu & mathumela band lyrics
[verse 1]
pomwe ndikufunitsitsa ndipamene wandisiya
ulibe nazo ntchito olo ntagwera mutu
suk*mva za munthu
koma ine wandisiya ndi ludzu
ndimafunabe pang’ono
pang’ono nk*makuphuzira
[refrain]
darlie tulo [?]
wandikhapila kosathwa
komano ndayesetsa ndafika potopa
ati sudzasiya kundikonda, k*mawuza anthu ena
tsono ngati umandikonda bwanji suli ndine?
tsono taleka ndikuwuze
[pre*chorus]
ndinakupilira mu nzinthu zambiri
zina zoyipa ndimamva titasiyana
koma ukati ulile bodza
uwonetsa kankhope ka m’ngelo
anzako ena ankandifunsiraso
ndilibe chipongwe chabe nd*nkakana
koma ukati undiyalutse anzako akuwona
[chorus]
basi
oh, basi ndileke
basi
oh, basi ndileke
[verse 2]
ngakhale pandekha osandilankhula (no)
ukakhalakhala osafusa za ine (no)
ukamagona usalote ine
(enough is enough, ine ndatopa)
unandichotsa mtima kuyika mwala
pano onse ondiwuza amandikonda
nkaw*ng’ana ndikulira
unandichotsera umunthu w*nga
tsiku osatha ndilire, ndilire, ndilire
[refrain]
ati sudzasiya kundikonda, k*mawuza anthu ena
tsono ngati umandikonda bwanji suli ndine?
tsono taleka ndikuwuze
[pre*chorus]
ndinakupilira mu nzinthu zambiri
zina zoyipa ndimamva titasiyana
koma ukati ulile bodza
uwonetsa kankhope ka m’ngelo
anzako ena ankandifunsiraso
ndilibe chipongwe chabe nd*nkakana
koma ukati undiyalutse anzako akuwona
[chorus]
basi
oh, basi ndileke
basi
oh, basi ndileke
basi
oh, basi ndileke
basi
oh, basi ndileke
Random Song Lyrics :
- aeon iii - born of osiris lyrics
- concentrați în metropole - paraziții lyrics
- two step - laura bell bundy lyrics
- marietta - the lone bellow lyrics
- okinawa - dashxxdash lyrics
- jedu kros - helena vondráčková lyrics
- prolific - drapht lyrics
- tell me - return lyrics
- molly - vild smith lyrics
- winter wonderland/christmas (baby please come home) [medley] - idina menzel lyrics