
malawi native anthem text - national anthem lyrics
Loading...
1.
mlungu dalitsani malawi,
mumsunge m’mtendere.
gonjetsani adani onse,
njala, nthenda, nsanje.
lunzitsani mitima yathu,
kuti tisaope.
mdalitse mtsogo leri na fe,
ndi mai malawi.
2.
malawi ndziko lokongola,
la chonde ndi ufulu,
nyanja ndi mphepo ya m’mapiri,
ndithudi tadala.
zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
n’mphatso zaulere.
nkhalango, madambo abwino.
ngwokoma malawi.
3.
o! ufulu tigwirizane,
kukweza malawi.
ndi chikondi, khama, k-mvera,
timutumikire.
pa nkhondo nkana pa mtendere,
cholinga n’chimodzi.
mai, bambo, tidzipereke,
pokweza malawi.
sent by carlos andré pereira da silva branco
Random Song Lyrics :
- m,m - barbie kills lyrics
- tomb of the dead - centinex lyrics
- stolz - ruffiction lyrics
- podrás contar conmigo - marta soto lyrics
- i ain't even know it - juke (lab tv) lyrics
- epilogue - airospace lyrics
- prom night - kade mcalli lyrics
- bipolar - kade mcalli lyrics
- roses - 2nd in command lyrics
- flowers (bos) - aries lyrics