
plan - praise umali lyrics
[verse 1: praise umali]
i worried all the time
i thought i’m running out of time
can’t take it a day at a time sometimes
man our dreams have been too loud since
we were only young kids
and now, we grown they loud still
i know ndizambiri umafuna mtima
nde pena mantha ankadzandigwila
like what if we don’t make it (yeah yeah)
what if we don’t make it (yeah yeah)
[chorus: praise umali]
koma tachoka nkutali
mulungu *n*li ndi pulani
pulani
inu zonse ndi nthawi
mulungu *n*li ndi pulani
pulani
yopanga za ifeyo (oooh oooh oooh)
yopanga za ifeyo
akupanga za ifeyo (oooh oooh oooh)
akupanga za ifeyo
[verse 2: gwamba]
yoh
venue yomweyo ena amaflopa
samatrenda nyimbo zawo akadropa
nde pena pride imafuna idzindikopa
koma mbuye w*nga sangakondwe kuti nzizipopa
nde rule number 1, k*makhala humble
poti ukazikweza amasiya kupanga zako
rule number 2, osakhala ndi tsankho
poti lero ndi kape mawa ali pamwamba pako
nkayang’ana k*mbuyo ngati ndingokuwa mbuye
ndinakhonza chani kuti inu mundimasule
mwandichotsa kutali kwinakunso mulambule
ulendowu ndiwautali koma
[chorus: praise umali]
koma tachoka nkutali
mulungu *n*li ndi pulani
pulani
inu zonse ndi nthawi
mulungu *n*li ndi pulani
pulani
yopanga za ifeyo (oooh oooh oooh)
yopanga za ifeyo
akupanga za ifeyo (oooh oooh oooh)
akupanga za ifeyo
Random Song Lyrics :
- bandbaz - farzan lyrics
- new pet - the living strange lyrics
- czyste ciało - lil blasti lyrics
- faaslon mein - sachet tandon lyrics - baaghi 3 lyrics
- streets of your town - dope lemon lyrics
- god dethroned - by your leave lyrics
- te la inventao - gordo master lyrics
- 50 tons de breu - suntizil lyrics
- good guys (feat. ao lexx & crokeyon10) - ao carlo lyrics
- 21 - doubledread lyrics