lirikcinta.com
a b c d e f g h i j k l m n o p q r s t u v w x y z 0 1 2 3 4 5 6 7 8 9 #

lirik lagu bona – jeg tellem

Loading...

yahman yah

tellem

zomwe ndik*maona

dziko li linagona

satana pano anangolowa paliponse kulimeza ngati chi ng’ona

akufalitsa ti mabodza

angofuna kuti pomboneza

eti uthenga wabho ena ati ndizanyasi mhhu muk*manyoza ah ah

koma sindingasiye ku praiser ine praiser ine eh

ndimamutsata yahweh ndipo ndimamupembeza ine mbeza ine hey

masten aziziwa mawu awo mawasungabe sungabe eh

uzikonda chauta
namalenga pokusunga iwe sunga iwe hey

devil yo k*mubona ahah

mpaka ak*magoma ahah

wak*mana ndi chiphona ah

sundikopa kopa ase

devil yo k*mubona mmhu

mpaka ak*magoma mmhu

wak*mana ndi chiphona

sundikopa kopa ase

ey yeah yah

ndipo sinkuopa ase

ey yeeh yah

sundikopa kopa ase
ey yeah yah

ndipo sinkuopa ase

ey yeah yah

kuyimba nako kukayamba kukoma

satana naye nde saku mapuma

akusaka tinjira atikole tizimupopa koma wagoma

nyengo zaka nazo zikayamba kusintha

ndipamene akufuna ndizifuntha

kenako nkhale desperate ndimutsate eti sindipanga izi ataaa

koma sindingasiye ku praiser ine praiser ine eh

ndimamutsata yahweh ndipo ndimamupembeza ine mbeza ine hey

masten aziziwa mawu awo mawasungabe sungabe eh
uzikonda chauta

namalenga pokusunga iwe sunga iwe hey

devil yo k*mubona ah ah

mpaka ak*magoma ah ah

wak*mana ndi chiphona ah

sundikopa kopa ase

devil yo k*mubona mmhu

mpaka ak*magoma mmhuu

wak*mana ndi chiphona

sundikopa kopa ase

ey yeay yah

ndipo sinkuopa ase

ey yeah yah

sundikopa kopa ase

ey yeah yah

ndipo sinkuopa ase

ey yeah yah

lirik lagu lainnya :

YANG LAGI NGE-TRENDS...

Loading...