lirik lagu chelele – molto zambia
verse 1
ndinapti n’kasakile ma ganyu /
ku lusaka amai tionane/
ndi guleko ma bikiloni a new/
k*mudzi ugh! kulije money/
talema kudyela munkhwani, chambo, kachumbari ndi bonongwe /
mundi sungile bwino bulu langa, nondi pemphelela kukacha ngwee /
a mesiya az’ingo dutsa nane, kwa ine pomwe ndi saka money /
for his blessings to shower me mu nthawi ya mvula ndi sanane /
lekani kulila amai chete, conde musa sakamane /
am about to make the family proud ndikhulupirira musadande /
ndi londole, ndi bodole, za banja langa n’kuti /
ndi bwela ndi galimoto agogo zolima n’kulonga mubuti /
apo ndishi ndine mponda matiki taleka n’fuula njuchi /
nati ni ponye sitepe ni chinje zinthu pakuti /
chorus
amama alulila mabvuto achuluka aza cita bwanji ehh /
linagoma chimbira, tsono thonje akuti azalima bwanji ehh /
tsiku ndi caka, mwеzi ndi zaka ng’ombe nazo zingo buula ehh /
nda langa k*mwamba conde malipiliro apa mwеzi ndi machenji ehh /
ooooh conde amama musalile /
ooooh conde adada zaine /
ooooh conde agogo musalile /
ooooh conde abanja zaine /
verse 2
yeo amama kodi k*mudzi bwanji uko /
boma inawa ninkha atata fataleza uko /
chabwino k*mva koma nane ndili bho /
pepa ninali chete, zii sini napange call /
papita mwezi khumi lomba, ndi kungo joba, ena aona ndi zoba /
pa lusaka umoyo lomba, kucita soka, abanja ndikali lova /
ayi conde sizipopa, mutu wokoka, ndilu kankha ngati rover /
yehovah ndikalu konkha, kopanda ku oonjoka, tsiku lina aza sova /
mphaka tonse mbanja lathu tika bvale nsuti /
nthawi zonse ndima uza amai n’kuti /
bridge
tsiku lina ndi zadya ndi mfumu /
pa mbale imodzi sauce chi phumu /
kunena yesu ndinu m’kulu /
ku dutsa mo jeda*jeda conde ndikuti /
chorus
amama alulila mabvuto achuluka aza cita bwanji ehh /
linagoma chimbira, tsono thonje akuti azalima bwanji ehh /
tsiku ndi caka, mwezi ndi zaka ng’ombe nazo zingo buula ehh /
nda langa k*mwamba conde malipiliro apa mwezi ndi machenji ehh /
ooooh conde amama musalile /
ooooh conde adada zaine /
ooooh conde agogo musalile /
ooooh conde abanja zaine /
lirik lagu lainnya :
- kumpulan lirik lagu pentatonix › lirik lagu do you hear what i hear – pentatonix
- kumpulan lirik lagu cultura profetica › lirik lagu pasiones, guerrillas y muerte (en vivo) – cultura profética
- kumpulan lirik lagu doxamillion › lirik lagu lost – doxamillion
- kumpulan lirik lagu daniel viglietti › lirik lagu la canción de pablo – daniel viglietti
- kumpulan lirik lagu elena goodrow › lirik lagu simpler time – elena goodrow
- kumpulan lirik lagu yungmex › lirik lagu hit it up! – yungmex
- kumpulan lirik lagu denz › lirik lagu splash – denz
- kumpulan lirik lagu tyler brown williams › lirik lagu never give up – tyler brown williams
- kumpulan lirik lagu makala › lirik lagu zebulon – makala
- kumpulan lirik lagu the grass roots › lirik lagu is it any wonder – the grass roots