lirikcinta.com
a b c d e f g h i j k l m n o p q r s t u v w x y z 0 1 2 3 4 5 6 7 8 9 #

lirik lagu nthawi – sagonjah & tadala

Loading...

[verse: tadala]
ukunyeka wa uwisi uzatani owuma
sakuwakuwa ndi galu oluma
nthawi ndi mambala, mankhwala
nthawi imakwilila mabala
tizaona pa mawa
zikapola
nthawi ikapyola
mafuta owalitsa ndikazola
misonzi mtima kusweka
maso ku nyeka abwenzi kuseka
dziko kunyenga
nkhondo pachibale
mpeni muchidale
oyenda naye ndiyemwe amakutchela ndale
yeah ndikudziwa ali pompa yudasi
kunalembedwa nde ndilibe nthumazi
sizingasinthe
siungazithe
mmene zilili ndi milili itatithe
nthawi kukana nthawi kulola
si nthawi yotaya,ndi nthawi yotola

lirik lagu lainnya :

YANG LAGI NGE-TRENDS...

Loading...